
Kufunika kochulutsa njira zopezera phindu la ndalama
1. TKufunika kochulutsa njira zopezera phindu la ndalama
Musicians in Malawi should explore multiple income streams to reduce their reliance on record sales and streaming revenue.
Mavuto a za chuma
Ntchito za oyimba mu Malawi zimakumana ndi zotsamwitsa, kuphatikizapo kulephera kufikira misika ya kunja komanso kujambula nyimbo popanda chilolezo. Kudalira njira zopezera ndalama zodziwika zokha kutha kukhala kovuta kwa anthu a luso.
Ubwino wa kuchulutsa njira
Kuchulutsa njira zopezera chuma, kumathandiza oyimba kuti akhale ndi mpata wopeza njira zopezera ndala zokhazikika makamaka mu nthawi yomwe ma lekodi awo akulidwa mwa apa ndi apo. Kumathandiziranso anthu a luso kutengerapo mwayi wotukula luso lawo komanso ukadaulo mu njira zosiyanasiya.